Saturday, April 20, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

Piksy Release New Song: Maloto

Piksy aka Chimfana Chodziwika Ndi Boma (CCNB) yesterday released his latest single, Maloto via www.malawi-music.com. Maloto finds Piksy in his rare element form linking up with producer of the moment Dj Sley (Chit Chat Records) to deliver a smooth track that is sure to keep music fans across Malawi and Africa singing and dancing into the wee hours of the morning.
In the song, Piksy is taken into the dream world where he impregnates his fiance and she gives birth to a bouncing baby boy who plainly resembles him.

In an interview with MacFarlane Mbewe, Piksy said, “Believe it or not, I literally had the wonderful dream. When I woke up in the morning I decided to compose a song. On whether or not my fiancé is pregnant that is worth discussing on a different forum.”

Maloto comes barely two weeks after Piksy released the smash hit Tsoka Liyenda which was also produced by Dj Sley. Tsoka Liyenda is built around a sample from the classic Tsoka Liyenda by the late Roward Gwirani. The music video for Tsoka Liyenda is expected to be out soon as Piksy prepares his new album.

Maloto Lyrics:

VERSE 1

I saw mwana wanga

What a cute baby

Proud dad anzanga anamva mbebe

Kusiyana ndi ana ena iye anali star

Ndinagwada kuthokoza Mbuye wodalitsa

Tinapita tonse kukagula ma dyper

Titagwirana manja pamalo panaipa

Tinakula koma we were getting tighter

Anthu otiyang’anan amadziwa

Timaitha

Nkhope yake inali brighter

Thupi lake linali lighter

Ndi nzeru anamudalitsa

Anatengera ine osakaika

Ndibwelere ndikagone (heh)

Mwina ndingalote nso (heh)

Ndingadzamukonde

Bola udzandibalire iweyoo

CHORUS

Ndinalota maloto otsekemera ine inde

Mwana wanga atafanana nawe Nde nde nde

Iwe

Ngati ndisadzuke

Usadzandikhumudwitse

Poti mtima wanga kukhala nawe wavomera

VERSE 2

Pali ponse

Anaoneka akalilombe

Ena anakondwa ena sanakondwe

Pawirife chikondi chinalipobe

Sichinachoke

Ndi za mbirimbiri

Zotilepheretsa kukhala awiri

Tiye tidzikondana mmene tiriri

Kunja kuli njoka wanga ndiwe basi

Ndikudziwa ndi zotheka eh

Kukonda iwe wekha eh

Chibwana ndaleka eh

Iwe mphete ndikuveka eh

Sweetie iwe ndine

Mphepo ingawombe tisasinthe

Limodzi tiwoloka mitsinje

Mpaka tikafike hey

Oh babie

CHORUS

Ndinalota maloto otsekera ine inde

Mwana wanga atafanana nawe Nde nde nde

Iwe

Ngati ndisadzuke

Usadzandikhumudwitse

Poti mtima wanga kukhala nawe wavomera

BRIDGE

No pain no gain

Kukusiya iwe no ways

Ngakhale asakondwe

Everything is gonna be okay

No pain no gain

Kukusiya iwe no ways

Ngakhale asakondwe

Everything is gonna be okay yeah

CHORUS

Ndinalota maloto otsekera ine inde

Mwana wanga atafanana nawe Nde nde nde

Iwe

Ngati ndisadzuke

Usadzandikhumudwitse

Poti mtima wanga kukhala nawe wavomera

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

4 COMMENTS

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles