Saturday, April 27, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Njuchi Day

Sat, 27 Apr 2024 10:00:00 UTC @ New Village House (Kampala Manase) - Elinationa And No Limit Presents Njuchi Day Music show with Njuchi Zitatu. The show will take place at New Village House in Manase on 27 April 2024 and it will have music performances b... More Info

Mzika Yaku America Yaphedwa Ku Nkhatabay

Mzika yaku Ameriaka Ya zaka  47 yomwe imapanga bisinesi ya phedwa ku nyumba yake m’bola ala Nkahatabay lachisanu sabala latha pa 20 july, 2018.

Omwalirayu amatchedwa Michael James Maglioli ndipo kwawo ndiku Massachusetts ndipo adaphedwa ku nyumba yake  yomwe ili m’mbali mwa nyanja ya Malawi.

M’neneri wa polisi Cecilia Mfune wanena kuti Michael amagulitsa mowa komanso zakumwa zozizilitsa ku khosi M’bomali.

Mayi ogwira ntchito zapa khomo pa bamboyo adena kuti iwo adamva munthu akugogoda ndipo  chitseko chidatsekulidwa poganiza kuti adali anthu ozagula zakumwa.

Mayiwo adali odabwa powona munthu wachilendo atavala chigoba ndipo adanyamula chikwanje.

Mbavazo zinanjata Michael kenako adamupha monvetsa chisoni.

Kafukufuku kuuchokera ku chipatala waonetsa kuti mzika yaku Americayi idafa chifukwa idataya magazi ambiri kudzera m’mabala omwe adali m’mutu mwake.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles