Friday, April 19, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Njuchi Day

Sat, 27 Apr 2024 10:00:00 UTC @ New Village House (Kampala Manase) - Elinationa And No Limit Presents Njuchi Day Music show with Njuchi Zitatu. The show will take place at New Village House in Manase on 27 April 2024 and it will have music performances b... More Info

“Malawi alibe zinthu zoyenelera pa chitukuko” – Mutharika

Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika wanena kuti dziko lino la Malawi lilibe zinthu loziyenereza kunkhazikitsa ntchito za chitukuko zomwe anthu ena akulonjeza kuti adzapanga ngati angawasankhe kunkhala atsogoleri a dziko lino.

A Muthalika apereka chitsanzo cha mwayi wa ntchito kwa anthu 1 Miliyoni m’chaka chimodzi komanso kunkhazikitsa mawulendo asitima za makono zomwe wachiwiri wawo a Dr Saulos Chilima wankhala akulonjeza.

Ndipo a Peter Munthalika anena kuti m’dziko muno mulibe mphamvu za magetsi okwanira kuchitira zitukuko.

Iwo alankhula izi dzuro pa m’sonkhano womwe adachititsa ku Nkhotakota pa ulendo wawo wobwerera ku Lilongwe kuchokera ku Mzuzu.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles