Thursday, April 25, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

TWO DPP HELICOPTERS TO LAND IN MALAWI SOON | #ChopperDown

Patadutsa nthawi yayitali pakumveka mphekesera zoti chipani cha Democratic Progressive (DPP) chagula ndege pokonzekera kampeni yamasankho omwe achitike chaka chamawa, chipanichi kudzera mwa m’neneri wake bambo Nicholas Dausi chafika poyera tsopano kutsimikiza zankhaniyi.

Malingana ndi bambo Dausi, chipani chawo cha DPP tsopano chamaliza kuchita dongosolo lonse loti ndegezi zomwe ndi ziwiri zamtundu wa ‘helicoptor’ zibwere m’dziko muno.

Bambo Dausi ati, DPP inagula kale ndegezi ndipo chomwe chatsala ndichakuti zibwere m’dziko muno koma iwo akana kunena tsiku lenileni lomwe ndegezi zitere panthaka ya Malawi.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

16 COMMENTS

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles