No featured image set for this post.
Malawi Post Cooperations (MPC) Robbed, K1.2m stolen at Malawi Housing Corporation
Published on July 3, 2013 at 12:13 PM by FACE OF MALAWI
Patangodutsa masiku ochepa mbava zitathyola office za Malawi Post Cooperations (MPC) ndikuba katundu wandalama zambiri, mbavazi zinabweleranso usiku wapitawu ndikukakatulanso ma office ena eight ndikuba katundu wambiri monga ma computer, camera ndi zina zambiri.
Chokhumudwitsa ndichakuti, mbavazi zisana kakatule ma office wa, zinayamba zakupa makofi ndi kumanga alonda a company ina ya ku UK omwe ndi amene amalondera malowa.