Thursday, April 25, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

“NDINE WOKONDWA TSOPANO” – CALLISTA.

Callista succeeds in removing Mutharika’s children as managers of K61bn estate
Former first lady Callista Mutharika has so far succeeded in her pursuit to remove former president Bingu wa Mutharika’s daughters, Duwa and Tapiwa as administrators of the controversial deceased’s estate.

Mkazi wa malemu Prof. Bingu Wa Muthalika ‘Callista’ wati, iye tsopano ndiwokondwa kuti Duwa ndi Tapiwa omwe amayendetsa chuma cha Bingu achotsedwa pa udindowu potsatira dandawulo lomwe iye anapereka ku bwalo lamilandu la High Court masiku apitawo.

Callista wati, panalibe chanzeru kuti anawa adziyendetsa chumacho popanda iye kutengapo gawo ngati mkazi wamalemu Prof. Bingu wa Muthalika, ndipo apa tsopano ndiwosangalala kuti asankha anthu ogwirizira chabe omwe adziyendetsa chumachi m’malo mwa iye ndi ana amalemuwa.

Anthuwa ndi Lawyer Kalekeni Kaphale yemwe adzithandizana ndi Modecai Mshisha m’malo mwa ana a malemu Muthalika ndipo iye( Callista) adziyimilidwa ndi bambo James Tomoka.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

1 COMMENT

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles