JOSEPHY KAMWENDO posts a picture of Nigerian team celebration Malawi win on Facebook

JOSEPHY KAMWENDO posts a picture of Nigerian team celebration Malawi win on Facebook

Published on September 9, 2013 at 10:33 PM by FACE OF MALAWI

102 words • approx. 1 min read

kodi zomwe wachita Josephy Kamwendo yemwenso ndi captain wa malawi national team popanga post chithuzi chomwe chikuonesa anyamata a Nigeria akukondwelera chigoli chawo m’mene amasewela ndi flames ndizolondola? kutengela kuti iye ndi captain.

kodi akanakamenya game imeneyi akanapanga zimenezi?
nanga kodi anasiidwa ndi yekha?
three words for JK .

Former Flames Captain, Joseph Kamwendo, who was dropped from the squad to face Nigeria due to undisclosed reasons by Coach Saintfeit has posted a picture on his facebook page of Nigeria Players celebrating one of their goals against the Flames.

Kamwendo wapangira izi chikuwawe akuti.

Ameneyu ndi psiru ndithu. Asazabwerenso kuno azikakhala ku Nigeria

Subscribe to our Youtube Channel: