Friday, May 3, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Mutharika abwelela kumudzi la mulungu

Pamene mphekesela yakula yoti msogoleli wa dziko lino Professor Peter Mutharika sakupeza bwino ndipo wagonekedwa mchipatala china ku United States of America, Nyumba ya boma yalengeza kuti Mutharika abwelela kumudzi la mulungu.

Izi zawika kuchokela mu uthenga omwe wasindikizidwa pasamba la Nyumba yofalitsa nkhani boma mdziko muno la Malawi Broadcasting Corporation (MBC 1).

Malingana ndi nyumbayi, uthenga wakubwela kwa a Mutharika wachokela kwa ofalisa nkhani ku nyumba ya chifumu yemwe ali ndi msogoleliyu ku New york, Mgeme Kalirani.

Kalirani wauza nyumbayi kuti Mutharika akuyembekezeleka kuzafika pa Kamuzu International Airport(KIA) ku Lilongwe 1 koloko masana.

Mukafuna kuziwa zambiri pa ulendowu pitilizani kuwelenga nkhani zathu

Related Posts

Robert Ngwira
Robert Ngwira
Attended Our Future Private Secondary School in Rumphi from 2006-2009 Holder of Diploma in Journalism from Malawi Institute of Journalism (MIJ) Hobbies, reading newspapers, going out with friends, listening to radio and watching football. Email: info@faceofmalawi.com

1 COMMENT

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles