Friday, March 29, 2024

Featured Video

Top 5 This Week

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Ku Malawi Kuli Luso

Ku Malawi kuli luso mtheradi, monga mukuona pa chithunzi chiri mmusimu, chikuonetsa pool table yomwe anakonza ndi ana achisodzera ku Monkey-Bay.

Tebuloyi ndi sampulo ya pool tabel yomwe ndiyodula kuigula kotero ana achicheperewa adaganiza zomanga tebuloyi kuti asamatayitse nthawi yawo pogwira ntchito za asodzi ku Monke-bay.

Tebuloyi ndiyomangidwa ndi njerwa, dothi, neti ndi mateyara okutha. Anawa adakonza tebuloyi potengera pool tabele yeni yeni.

M’modzi mwa anawa dzina lake Vinicent adaganiza zo konza chinthuchi ndipo payekha sakadakwanitsa kotero adauza amzake kuti akonze chinthuchi.

pakadali pano anawa amakhala mosangala kamba masewero amaseweredwa pa tebulo amabweretsa chisangalaro pakati pawo.

Ukadaulo oterewu umabweretsa msangulotso pa kati pa ana. Monga tebulori likuonekera mutha  kuona kuti likufanana ndi pool table ili pachithunzi m’munsi.

 

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles