Thursday, April 25, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

M’dala wina wanjatidwa kamba kojandula mwana wa zaka zitatu

Apolisi ku Chikwawa anjata m’dalala wa zaka makumi awiri ndi zitatu kamba kokuba mwana wazakazitatu ndikumu jadula (m’dulidwe) popanda chilorezo cha makolo amwanayo.

Mneneri wa polisi, Constable Foster Benjamin, wanena kuti mkuluyi dzina lake ndi Symon Kayiya ndipo amazitcha Ngaliba potengera chikhalidwe chake.

“Kayiya ananyengerela mwanayi ndi ndalama kuti akamugulira filizesi ndipo adatengela mwanayu pa tchile pomwe adagwiritsa ntchito mphanvu pa mdulidwe wa mwanayu” Costable Benjamin adalongosola motero.

Ndipo mwanayu adafooka kwambiri kamba adakakamizidwa kuti amwe phala la moto.

Izi zidachititsa makolo a mwanayo kutsina khutu apolisi pa nkhaniyi. Ndipo Kayiya wanjatidwa ali muchitolokosi cha polisi ku  Chikwawa.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles