Thursday, March 28, 2024

Featured Video

Top 5 This Week

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Mphenzi Ipha Munthu Ku Mangochi

Mphenzi yaomba nyumba ndipo yapha mwana wa za zisanu ndi chimodzi wa m’mudzi mwa a Jalasi m’boma la Mangochi ndipo mphenziyi yapweteka nyamata wa zaka khumi ndi ziwiri wa m’mudzi momwemo.

Ngoziyi yachitika pa 27 November, 2018 m’munthawi ya 5 koloko madzulo m’mudzi mwa Balakasi.

Shanila Saidi wazaka makumi atatu ndi zisanu, yemwe ali mayi wa anawa adawuza apolisi panthawiyo kuti kunali mvula yambiri yomwe imagwa mophatikiza ziphaliwali (Mphenzi) ndipo izi zidachititsa anawa kuti kuti akause m’nyumba.

“Izi zidachitika pomwe mwanayo amakodza kudzera pa zenera la nyumbayo ndipo mphenzi idaomba ndikupha mwanayo pa malo omwewo ndi ku vulaza mwana m’modzi.” Mayi Saidi adatero.

 

 

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles