Friday, April 19, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

Zosiyilana! Chilima Asiyira Chimulirenji

Mawu a wachiwiri wakale wamtsogoleri wadziko lino a Saulos Chilima okuti utsogole ndi osiyirana, apherezera.

Mawuwa apherezera pomwe a Chilima Asiyira a Everton Chimulirenji ofesi ya wachiwiri kwamtsogoleri wadziko lino.

Mumisonkhano yawo yokopa anthu a Chilima akhale akunena kuti ntchito ya utsogoleri si ya munthu mmodzi koma ndiyosiyirana.

Izi zachitika chomwechi kutsatira kulengeza kwa bungwe loona za chisankho mdziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) kuti A Peter Mutharika ndi omwe apambana pa mpando wa mtsogoleri wadziko lino motsatiridwa ndi a Everton Chimulirenji ngati wachiwiri wawo.

Wamkulu wa pampando wabungwe loona za chisankho mdziko muno Justice Dr. Jane Ansah anafunira mafuno abwino a Mutharika ndi a Chimulirenji kutsatira kupambana kwawo pa zisankhozi.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Flora Mitumba
Flora Mitumba
Email: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles