Saturday, April 20, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

AKOMOKA ATAMWA ZOONJEZELA MPHAMVU KUBEDI

Nkulu wina yemwe dzina lake silikudziwika wokonda khalidwe lopanga chisembwele ndi azimayi oyenda yenda[Mahule],waona mbwadza atakoma atamwa makhwala owonjezela mphamve kubedi pokonzekela mzimayi wina yemwe anagwilizana naye.

Malingana ndi tsamba la nchezo lapa intaneti lotchedwa facebook,Nkuluyi akuti anagwiliza ndi m’mayi wina kuti akumane malo ena ogona alendo ntaunimu.Ndipo podikila nkuluyu anamwa makhwala owonjezela mpamvu kubedi otchedwa nkwapukwapu.

Tsoka ilo mbendu anagwizananayo ija inapezeka kuti sinabwele ku malo ogona alendo anagwilizanawo,kotelo kuti nkuluyi zinamuvuta mpaka anakomoka nawo makhwalawo poti sanagwile ncthito yake bwinobwino.

M’musimu ndi zina mwa zithuzi zomwe zili pa tsamba la nchezo la intaneti  lotchedwa facebook  za nkuluyi ndi ena omwe anamupeza nkuliyu

.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Mc Noel Kasinja
Mc Noel Kasinjahttps://faceofmalawi.com
A writer,Analyst and Music Promoter. Email: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles