Tuesday, April 30, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Fact Up Night

Sat, 04 May 2024 20:00:00 UTC @ Club Casaulina - On 4th May 2024 Achina Gattah Ase and Gibo Pearson will be performing live for Fact Up Night at Club Casaulina in Lilongwe Area 25. The event will start from 8 PM till late More Info
Kapadocia Live In Mzuzu

Sun, 05 May 2024 13:00:00 UTC @ Rose Chanaichi's Gardens - Kapadocia will be performing live in Mzuzu Area 4 at Rose Chanaichi's Gardens on 05 May 2024. He will be supported by Rose Chanaichi Kayira, Motte Jez, Esther Mashani, Chipha Dada, Dele... More Info

Mzika Yaku America Yaphedwa Ku Nkhatabay

Mzika yaku Ameriaka Ya zaka  47 yomwe imapanga bisinesi ya phedwa ku nyumba yake m’bola ala Nkahatabay lachisanu sabala latha pa 20 july, 2018.

Omwalirayu amatchedwa Michael James Maglioli ndipo kwawo ndiku Massachusetts ndipo adaphedwa ku nyumba yake  yomwe ili m’mbali mwa nyanja ya Malawi.

M’neneri wa polisi Cecilia Mfune wanena kuti Michael amagulitsa mowa komanso zakumwa zozizilitsa ku khosi M’bomali.

Mayi ogwira ntchito zapa khomo pa bamboyo adena kuti iwo adamva munthu akugogoda ndipo  chitseko chidatsekulidwa poganiza kuti adali anthu ozagula zakumwa.

Mayiwo adali odabwa powona munthu wachilendo atavala chigoba ndipo adanyamula chikwanje.

Mbavazo zinanjata Michael kenako adamupha monvetsa chisoni.

Kafukufuku kuuchokera ku chipatala waonetsa kuti mzika yaku Americayi idafa chifukwa idataya magazi ambiri kudzera m’mabala omwe adali m’mutu mwake.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles