Thursday, May 2, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Madzi Ayamba ku vuta Ku Lilongwe

Anthu okhala mu m’zinda wa Lilongwe ayembekezere kuvuta kwamadzi miyezi ikubwerayi.

Lilongwe Watete Board (LWB) anena kuti madzi ndiochepa ku Damu losungila ku Kamuzu Dam. izi zikhala chomwechi kamba kakuchepa kwa mvula m’chakachi.

Wamkulu oyang’anila Lilongwe Water Board Alfonso Chikuni wanena kuti Damuli lidango dzadza ndika mlingo kochepa kokha kotero madera ambiri ku Lilongwe samalandira madzi mokwanira.

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles