Saturday, April 27, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Mzuzu Shutdown Music Bash

Sat, 27 Apr 2024 17:30:00 UTC @ Chisanga Complex Center (Mzuni Road) - Thoms Park Events Presents "Mzuzu Shutdown Music Bash' with live performances by The Black Missionaries Band, Anthony Makondetsa,Moda Fumulani, Khozie Masimbe, Yanjanani Chumbu, Pop You... More Info

“Ntchito Yofalitsa za Matenda a Shuga ikubwerela M’mbuyo” – Diabetes association of Malawi

Bungwe la anthu omwe amadwala matenda a Shuga lati kuchepa kwa zipangizo zofalitsira mauthenga a nthendayi m’madera akumidzi ndi chimodzi mwa zinthu zomwe zikubwenzeretsa mmbuyo ntchito yolimbana ndi nthendayi.

Mtsogoleri wa Bungweli, a Clement Mandala anena izi pomwe dziko la Malawi pamodzi ndi mayiko onse padziko lapansi akukumbukira tsiku loganizira za matenda a Shuga pa 14 November chaka chilichonse.

A Mandala anati ndizomvetsa chisoni kuti anthu ambiri akudwala komanso kumwalira ndi matendawa kaamba kosowa upangiri wa momwe angapewere nthendayi.

Source : Yoneco Fm

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles