Monday, April 29, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Fact Up Night

Sat, 04 May 2024 20:00:00 UTC @ Club Casaulina - On 4th May 2024 Achina Gattah Ase and Gibo Pearson will be performing live for Fact Up Night at Club Casaulina in Lilongwe Area 25. The event will start from 8 PM till late More Info
Kapadocia Live In Mzuzu

Sun, 05 May 2024 13:00:00 UTC @ Rose Chanaichi's Gardens - Kapadocia will be performing live in Mzuzu Area 4 at Rose Chanaichi's Gardens on 05 May 2024. He will be supported by Rose Chanaichi Kayira, Motte Jez, Esther Mashani, Chipha Dada, Dele... More Info

TWO DPP HELICOPTERS TO LAND IN MALAWI SOON | #ChopperDown

Patadutsa nthawi yayitali pakumveka mphekesera zoti chipani cha Democratic Progressive (DPP) chagula ndege pokonzekera kampeni yamasankho omwe achitike chaka chamawa, chipanichi kudzera mwa m’neneri wake bambo Nicholas Dausi chafika poyera tsopano kutsimikiza zankhaniyi.

Malingana ndi bambo Dausi, chipani chawo cha DPP tsopano chamaliza kuchita dongosolo lonse loti ndegezi zomwe ndi ziwiri zamtundu wa ‘helicoptor’ zibwere m’dziko muno.

Bambo Dausi ati, DPP inagula kale ndegezi ndipo chomwe chatsala ndichakuti zibwere m’dziko muno koma iwo akana kunena tsiku lenileni lomwe ndegezi zitere panthaka ya Malawi.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

16 COMMENTS

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles