Saturday, May 4, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Mutharika asankha wankulu wa bungwe lazachisankho la MEC

President Peter Mutharika wasankha Justice Jane Ansah kukhala wapampando wa bungwe lazachisankho la Malawi Electoral Commission (MEC).

Ansah walowa m’malo mwa malemu Maxon Mbendera omwe anamwalira mwezi watha atangogwa pa mpando ku Lilongwe akugwila nchito zina zokhuza ofesi yake.

Mlembi wamkulu wa boma a George Mkondiwa ati kusankhudwaku kukuyambila lero.

Justice Ansah anali judge ku bwalo la apilo.

Related Posts

Robert Ngwira
Robert Ngwira
Attended Our Future Private Secondary School in Rumphi from 2006-2009 Holder of Diploma in Journalism from Malawi Institute of Journalism (MIJ) Hobbies, reading newspapers, going out with friends, listening to radio and watching football. Email: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles