Saturday, May 4, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

MUNTHU ANABA MA DEGREE A BAMBO PHOYA WAPEZEKA

Apolisi ku Blantyre, akusunga m’chitolokosi munthu yemwe akumuganizila kuti, anaba ndalama zokwana K20,000 ndi ma degree awiri kunyumba ya Nduna yowona za malo ndi zomangamanga bambo Henry Phoya kunyumba yawo yawo ku Chigumula.

Malingana ndi report lomwe latipeza, munthuyu ati anali wantchito wa ku nyumba ya bambo Phoya koma anangothawa ndi ndalama komanso ndi degree ya olemekeza wa pamodzi ndi ya akazi awo.

Related Posts

2 COMMENTS

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles