KASAMBARA WARNS VICE PRESIDENT – ”NDIKUTIBULANI BECAREFUL”

KASAMBARA WARNS VICE PRESIDENT – ”NDIKUTIBULANI BECAREFUL”

Published on June 30, 2013 at 6:54 PM by FACE OF MALAWI

64 words • approx. 1 min read

Nduna yadzachilungamo mdziko muno ‘Ralph Kasambara’ yachenjeza wachiwiri kwa President wadziko lino bambo Khumb Kachali kuti amugulura mano akapitiliza zomamukhomelera.

Chidani cha mamulumuzanawa, chidayamba kuchokera pomwe Kachali adakaniza Kasambara contract yonyamula fetereza wa ‘Subsidy’ ndipo kuti m’malo mwake, adangophangira yekha.

Kuchokera apa, makosanawa sayang’anizana diso la bwino ndipo mphekesera yomwe yatipeza ndiyakuti Kasambara wachenjeza mkuluyu kuti amutidzimula ngati, angapitilize kumamukhomelera kwa JB chifukwa zamukwana.

Subscribe to our Youtube Channel: