
Ma Black Akana Kulandira “Banzi” Lo Chokera Ku Dpp
Published on July 27, 2018 at 10:04 AM by Face of Malawi
Mphekesera ikumveka kuti Ma blacks (Black Missionaries) akuti dzulo akana kulandira ndalama zoti akamenye show ya ulere la mulungu Ku Blantyre pofuna kuti anthu ambiri asazapite Ku sonkhano wa UTM
Ma report akusonyeza kuti Ma blacks ayankha kuti Ali ndi show ina ndipo sangawawuze zochita mu masiku ochepa kuti akaimbe pa mwambo wo tsegulira Kamuzu stadium.
Zikumveka kuti m’modzi mwa oyimba amene amafuna akathandizane ndi ma blacks anasankhidwa ndi katswiri Taygrin.
More to come…..