Saturday, April 27, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Njuchi Day

Sat, 27 Apr 2024 10:00:00 UTC @ New Village House (Kampala Manase) - Elinationa And No Limit Presents Njuchi Day Music show with Njuchi Zitatu. The show will take place at New Village House in Manase on 27 April 2024 and it will have music performances b... More Info

Kathyali Wina Wanjatidwa kamba kokuba Katundu wa K2 millioni

Apolisi mtowinshipi ya Limbe ku Blantyre anjata kathyali wina kamba kukoba katundu okwana ndalama k2.2 million ndipo mkuyuyu dzina lake ndi Blessings Mtitule.

M’neneri wa polisi wa ku Limbe  Widson Nhlane wanena kuti analandila uthenga ku Chokera kwa anthu okhala ku Chinyonga pa 18 July, 2018 kuti mbava zathyola nyumba ya Mai wina ndipo zinaba makina akomputa, iphone, masipika komaso nsapato zachizibambo zokwana 12 ndi zovala zokwana k2,240,000.

Apolisi atapanga chipikisheni pa 23, Mtitule ananjatidwa ndipo anamupeza ndi katundu yemwe wa tchulidwayi.

Mneneri wa polisiyu wanena kuti adakali kalikiliki kufufuza kandundu otsala yemwe adabebwayo.

Pakadali pano apolisi amema anthu amderali kuti asanyozere kutsina khutu apolisi pankhani ya zimbalangondozi akaziona.

Mtitule amakhala m’mudzi mwa Mtalala, mfumu yaikule Nsomba ku Blantyre ndipo akuyembekera kukalowa Court sabata la mawa.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles