Tuesday, April 30, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Anyamata Asanu Akabaza anjatidwa kamba kosalipira Msonkho

Anyamata akabaza omwe amachita ziwonesero kamba kosakondwa ndi zoti azilipila sonkho pamwezi awanjata m’boma la Salima.

Anyamata okwana 5 awamanga Ku Salima kamba kosalipila ndalama ya sonkho womwe amadula pamwezi kamba kopanga bisinesi ya kabaza

Anyamata anjinga zakabazawa mwezi uliwose amapeleka K3500 Ku Boma ndicholinga Boma lizigwirisa ndalamayi pa nkhani zachitukuko.

Akabaza anadandaula kuti ndikovuta kupanga K3500 yongowapasa a boma popeza iwo kupeza Chakudya kuzera mukabaza akumachita kuchivutikila.

Pakadali pano Boma lawalanda njinga akabaza osakwanisa kulipila sonkho m’bomali.

Zambiri za nkhaniyi tikupatsirani ka nthawi kena.

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles