MASSA ladandaula ndi FAM pomuyitana Gabadinho Mhango ku camp ya Flames kukhonzekela Zimbabwe

MASSA ladandaula ndi FAM pomuyitana Gabadinho Mhango ku camp ya Flames kukhonzekela Zimbabwe

Published on May 29, 2013 at 1:14 AM by FACE OF MALAWI

106 words • approx. 1 min read

Bungwe la Malawi Schools Sports Association (MASSA) ladandaula ndizimene anapanga a FAM pomuyitana Gabadinho Mhango ku camp ya Flames komanso pomulowetsa game ya Zimbabwe.

”The game was a friendly one. Gaba is a Form 2 kid. He is suppossed to be in school studying and not playing football. Why FAM called him into camp is just inconsiderate to his future. A FAM akupangilanji zimenezi. Kodi akufuna kuti akanike kulemba mayeso ngati chaka chathanso?” adandaula a MASSA

”kodi nawo a MASSA angothi mfwii mfwiii panopa pamene Gaba yo adasewera kale masewero wo bwanji? Samanena atamutenga ku camp ko bwanji?” a John Kaputa a FAM adabwa motero

Subscribe to our Youtube Channel: