Thursday, May 2, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

A DPP A WOTCHA SUKULU YA JOYCE BANDA

Akuluakulu a chipani cholamula boma cha PP ati, sakupenekera konse kuti moto womwe watentha ma hostel anyamata pa sukulu ya Joyce Banda Foundation yaku Chimwankhunda ku Blantyre, anayatsa ndi a chipani cha DPP.

”ife sitikupenekera konse kapena kuchotsera kuti anachita zawupanduzi ndi achipani cha DPP chifukwa sakugona tulo ndi Mayi Joyce Banda. Akufunafuna njira zoti awagonjetse koma akulephera ndinkuwona achita izi. Koma ndiiiiiithu, anjatidwa posakhalitsa pamodzi ndi amene akuwatumayo” ayankhula chonchi mamulumuzanawa.

Related Posts

1 COMMENT

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles