Tuesday, March 19, 2024

Featured Video

Top 5 This Week

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

“Ntchito Yofalitsa za Matenda a Shuga ikubwerela M’mbuyo” – Diabetes association of Malawi

Bungwe la anthu omwe amadwala matenda a Shuga lati kuchepa kwa zipangizo zofalitsira mauthenga a nthendayi m’madera akumidzi ndi chimodzi mwa zinthu zomwe zikubwenzeretsa mmbuyo ntchito yolimbana ndi nthendayi.

Mtsogoleri wa Bungweli, a Clement Mandala anena izi pomwe dziko la Malawi pamodzi ndi mayiko onse padziko lapansi akukumbukira tsiku loganizira za matenda a Shuga pa 14 November chaka chilichonse.

A Mandala anati ndizomvetsa chisoni kuti anthu ambiri akudwala komanso kumwalira ndi matendawa kaamba kosowa upangiri wa momwe angapewere nthendayi.

Source : Yoneco Fm

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles