Saturday, April 27, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Njuchi Day

Sat, 27 Apr 2024 10:00:00 UTC @ New Village House (Kampala Manase) - Elinationa And No Limit Presents Njuchi Day Music show with Njuchi Zitatu. The show will take place at New Village House in Manase on 27 April 2024 and it will have music performances b... More Info

Mkulu wina wadzinjata M’boma la Mzimba

Mkulu wina wa zaka 63 wadzinjata m’boma la Mzimba.

Mkuluyi amadziwika ndi dzina loti Davison Kumwenda ndipo amakhala m’dela la Mfumu yaikulu M’mbelwa ku Mzimba.

M’neneri wa polisi Peter Botha wanena kuti Kumwenda anachoka kunyumba kwake osatsanzika anthu apakhoma lake.

Ndipo masana wake bambo Kumwenda adawapeza atadzinjata mu mtengo wamango pafupi ndi nyumba yawo.

Botha adaonjezera ponena kuti Kumwena anali pa mkangano wa malo ndi anthu apachibale ndipo amfumu am’mudzimo amayendetsa nkhani ya malo.

Imfa ya bambo kumwenda yachitika patangotha masiku ochepa pomwe bambo wina wazaka 45 Josted Saka atadzinjataso m’boma la Mzimba.

 

 

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles