Monday, April 29, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Fact Up Night

Sat, 04 May 2024 20:00:00 UTC @ Club Casaulina - On 4th May 2024 Achina Gattah Ase and Gibo Pearson will be performing live for Fact Up Night at Club Casaulina in Lilongwe Area 25. The event will start from 8 PM till late More Info
Kapadocia Live In Mzuzu

Sun, 05 May 2024 13:00:00 UTC @ Rose Chanaichi's Gardens - Kapadocia will be performing live in Mzuzu Area 4 at Rose Chanaichi's Gardens on 05 May 2024. He will be supported by Rose Chanaichi Kayira, Motte Jez, Esther Mashani, Chipha Dada, Dele... More Info

Ndili ndi Kuthekera Kotukula Dziko La Malawi – Muluzi

Mtsogoleri wa Chipani chotsutsa cha United Democratic Front (UDF), Atupele Muluzi wati iye ali ndi kuthekera konse kotukula dziko la Malawi.

Muluzi in the middle

Muluzi wayankhula izi lachitatu lapitali pa msonkhano waukulu omwe chipani chake chidapangaitsa ku Blantyre pokonzekera zisankho zomwe zili nkudzazi.

“Ndimakonda dziko la Malawi ndipo ndili ndi masomphenya osintha zinthu. Ndimakhulupilira kuti kusintha ndikotheka pokha pokha ife ayini ake titaikirapo chidwi,” atero a Muluzi.

A Muluzi anonjezera kunena kuti ulimi wa fodya siukubweresaso phindu lokwanira choncho dziko la Malawi langoyenera kupeza njira zina zobweretsera chuma.

Ena omwe anayankhula ku msonkhanowo ndi mtsogoleri wakale wa dziko lino Dr Bakili Muluzi omwe anati nthawi yatha tsopano kuti atsogoleri azipani azilimbana ndi ndale zokokanakokana.

Iwo anapereka chitsaonzo cha mkazi wa mtsogoleri wakale wadziko lino, Callista Mutharika omwe mbuyomu m’mawu awo adanena anthu ena ochita ndale kuti ndi matchona ati kamba koti adakhalitsa kwambiri m’maiko akutali.

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles