Sunday, May 5, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

[showmfm]

Upcoming Events

[showevents]

Asilikari Anayi Aku Malawi Adasowa Ku DRC

Asilikari anayi a Malawi Defence Force adasowa pamene asilikari ena okwana asanu ndi m’modzi adaphedwa m’dziko la DRC sabata latha.

Sergeant Chancy Mwakawenga, Sergeant Boniface Noah, Corporal Geoge Salimu ndi Lance Corporal Gift sakupezeka kuchokera pa 13 November, 2018.

Wachiwiri kwa unduna wa za Chitetezo, Amos Mailos, wanena izi ku Parliament pa 23 November, 2018, Chaku m’mawa ndipo akukambirana za asilikari anayi adasowa ku DRC.

 

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles