”ANAWA ANDIYENDA NJOMBA” – CALLISTA.

Date:

Mkazi wa malemu Professor Bingu wa Muthalika ‘Calista’ wati iye, sakukayika konse kuti ana amalemu Bingu, anabisa ‘Will’ yomwe mkuluyu analemba atakwatirana naye.

Calista wati, akukhulupilira zoti m’mene ankakondanirana ndi mwamuna wake, sangamusiye osamuyika pa will koma kuti achina Duwa ndiwomwe anataya will yi mwadala ndicholinga chofuna kumukhawulitsa.

Mayiyu wati, akamang’ala ku bwalo lamilandu kuti will yomwe ilipo panopayi, ikhale yopanda ntchito ndipo kuti, chuma cha Bingu, iyenso apeze nawo gawo ngati mkazi wake.

Subscribe to our Youtube Channel:

3 COMMENTS

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Share post:

Featured Video

click to play

Popular

More like this
Related

Elderly Woman Found Dead in Ntchisi Hills After Two-Day Disappearance

The body of an old woman has been found...

Drama As Unknown Man Invade Rihanna’s House To Propose To Her

A yet-to-be identified man who travelled to Los Angeles...

Student found dead in girlfriend’s house in Zambia

WHILE his parents thought he was in boarding school...

Government calls civil servants in financial contribution Support towards cyclone victims

Government has appealed to civil servants to make financial...