Thursday, April 25, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Zomba City Festival

Fri, 26 Apr 2024 10:00:00 UTC @ Botanic Garden - 2024 Zomba City Festival is schedulled to take place on 26 to 28 April at Botanic Garden in Zomba This is a festival for all ages in the historic mountain city of Zomba. Celebrate Cultu... More Info
Queens Club Shut Down

Fri, 26 Apr 2024 19:00:00 UTC @ Queens Club - Queens Club Presents "Queens Club Shut Down" with music performances by Kelly Kay, Charisma, Teddy Makadi and Praise Umali. The show will take place at Queens Club in Mzuzu on 26 April... More Info

Mkulu Wina Wamwalira Kamba ka Bibida

Mkulu wina wazaka makumi anayi ndi ziwiri odziwika ndi dzina la Dickson Ulaya wamwalira kamba ka mowo wakachaso poti sadadye kalikonse.

M’neneri wa polisi ku Mangochi, Amina Tepani, wanena kuti izi zinachitika masana a lachitatu ku Matapwata Shabin ku Mangochi.

“Atangolandila ndalama za mwezi wa Sepitemba sabata lathali, mkuluyi wakhala asakupita ku ntchito ndipo iye wakhala akumwa Kachaso muma shabini osiyana siyana ku Mangochi” Amina adatero.

Dickson amagwira ntchito ku Agriculture ndipo amayang’anila ziweto.

Mkuluyi anakomoka atamwa mowa wambiri osadyera, kenako anthu achisoni adamutengela kuchipatala cha Mangochi.

Dickson amachokera ku Kambeta m’mudzi mwa mfumu yaikulu Mlumbe ku Zomba.

 

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles