Monday, April 29, 2024

Featured Video

Latest Stories

Top 10 Music

Upcoming Events

Fact Up Night

Sat, 04 May 2024 20:00:00 UTC @ Club Casaulina - On 4th May 2024 Achina Gattah Ase and Gibo Pearson will be performing live for Fact Up Night at Club Casaulina in Lilongwe Area 25. The event will start from 8 PM till late More Info
Kapadocia Live In Mzuzu

Sun, 05 May 2024 13:00:00 UTC @ Rose Chanaichi's Gardens - Kapadocia will be performing live in Mzuzu Area 4 at Rose Chanaichi's Gardens on 05 May 2024. He will be supported by Rose Chanaichi Kayira, Motte Jez, Esther Mashani, Chipha Dada, Dele... More Info

Mkulu Wina Wamwalira Kamba ka Bibida

Mkulu wina wazaka makumi anayi ndi ziwiri odziwika ndi dzina la Dickson Ulaya wamwalira kamba ka mowo wakachaso poti sadadye kalikonse.

M’neneri wa polisi ku Mangochi, Amina Tepani, wanena kuti izi zinachitika masana a lachitatu ku Matapwata Shabin ku Mangochi.

“Atangolandila ndalama za mwezi wa Sepitemba sabata lathali, mkuluyi wakhala asakupita ku ntchito ndipo iye wakhala akumwa Kachaso muma shabini osiyana siyana ku Mangochi” Amina adatero.

Dickson amagwira ntchito ku Agriculture ndipo amayang’anila ziweto.

Mkuluyi anakomoka atamwa mowa wambiri osadyera, kenako anthu achisoni adamutengela kuchipatala cha Mangochi.

Dickson amachokera ku Kambeta m’mudzi mwa mfumu yaikulu Mlumbe ku Zomba.

 

Subscribe to our Youtube Channel:

Related Posts

Face of Malawi
Face of Malawihttps://www.faceofmalawi.com
For more Info: info@faceofmalawi.com

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles